Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

Uthenga Wabwino Wolembedwa ndi Mateyu

Machaputala

Mitu

  • 1

    • Mzere wa makolo a Yesu Khristu (1-17)

    • Kubadwa kwa Yesu (18-25)

  • 2

    • Okhulupirira nyenyezi anapita kukamuona (1-12)

    • Anathawira ku Iguputo (13-15)

    • Herode anapha ana aamuna (16-18)

    • Anabwerera ku Nazareti (19-23)

  • 3

    • Yohane Mʼbatizi ankalalikira (1-12)

    • Ubatizo wa Yesu (13-17)

  • 4

    • Mdyerekezi anayesa Yesu (1-11)

    • Yesu anayamba kulalikira ku Galileya (12-17)

    • Anasankha ophunzira oyambirira (18-22)

    • Yesu ankalalikira, kuphunzitsa komanso kuchiritsa (23-25)

  • 5

    • ULALIKI WAPAPHIRI (1-48)

      • Yesu anayamba kuphunzitsa paphiri (1, 2)

      • Zinthu 9 zimene zimapangitsa anthu kuti azikhala osangalala (3-12)

      • Mchere komanso kuwala (13-16)

      • Yesu anakwaniritsa Chilamulo (17-20)

      • Malangizo okhudza mkwiyo (21-26), chigololo (27-30), kutha kwa ukwati (31, 32), malumbiro (33-37), kubwezera (38-42), kukonda adani athu (43-48)

  • 6

    • ULALIKI WAPAPHIRI (1-34)

      • Muzipewa kudzionetsera kuti ndinu olungama (1-4)

      • Mmene tingapempherere (5-15)

        • Pemphero la chitsanzo (9-13)

      • Kusala kudya (16-18)

      • Chuma padziko lapansi komanso kumwamba (19-24)

      • Siyani kuda nkhawa (25-34)

        • Nthawi zonse muziika Ufumu pamalo oyamba (33)

  • 7

    • ULALIKI WAPAPHIRI (1-27)

      • Siyani kuweruza (1-6)

      • Pitirizani kupempha, kufunafuna, kugogoda (7-11)

      • Muzichitira anthu zimene mukufuna kuti akuchitireni (12)

      • Geti lalingʼono (13, 14)

      • Amadziwika ndi zipatso zawo (15-23)

      • Nyumba yapathanthwe, nyumba yapamchenga (24-27)

    • Gulu la anthu linadabwa ndi kaphunzitsidwe ka Yesu (28, 29)

  • 8

    • Anachiritsa munthu wakhate (1-4)

    • Chikhulupiriro cha mtsogoleri wa asilikali (5-13)

    • Yesu anachiritsa anthu ambiri ku Kaperenao (14-17)

    • Zimene tingachite kuti tizitsatira Yesu (18-22)

    • Yesu analetsa mphepo yamphamvu (23-27)

    • Yesu anatumiza ziwanda munkhumba (28-34)

  • 9

    • Yesu anachiritsa munthu wakufa ziwalo (1-8)

    • Yesu anaitana Mateyu (9-13)

    • Funso lokhudza kusala kudya (14-17)

    • Mwana wamkazi wa Yairo; mzimayi anagwira chovala chakunja cha Yesu (18-26)

    • Yesu anachiritsa munthu wosaona komanso wosalankhula (27-34)

    • Zokolola nʼzochuluka, koma antchito ndi ochepa (35-38)

  • 10

    • Atumwi 12 (1-4)

    • Malangizo okhudza kulalikira (5-15)

    • Ophunzira adzazunzidwa (16-25)

    • Muziopa Mulungu, osati anthu (26-31)

    • Osati mtendere, koma lupanga (32-39)

    • Kulandira ophunzira a Yesu (40-42)

  • 11

    • Yohane Mʼbatizi analemekezedwa (1-15)

    • Anadzudzula mʼbadwo wosamvera (16-24)

    • Yesu anatamanda Atate wake chifukwa chokomera mtima anthu wamba (25-27)

    • Goli la Yesu limatsitsimula (28-30)

  • 12

    • Yesu ndi “Mbuye wa Sabata” (1-8)

    • Anachiritsa munthu wolumala dzanja (9-14)

    • Mtumiki amene Mulungu amamukonda (15-21)

    • Anatulutsa ziwanda pogwiritsa ntchito mzimu woyera (22-30)

    • Tchimo losakhululukidwa (31, 32)

    • Mtengo umadziwika ndi zipatso zake (33-37)

    • Chizindikiro cha Yona (38-42)

    • Mzimu wonyansa ukabwerera (43-45)

    • Amayi ake a Yesu komanso azichimwene ake (46-50)

  • 13

    • MAFANIZO OKHUDZA UFUMU (1-52)

      • Wofesa mbewu (1-9)

      • Chifukwa chake Yesu ankagwiritsa ntchito mafanizo (10-17)

      • Tanthauzo la fanizo la wofesa mbewu (18-23)

      • Tirigu ndi namsongole (24-30)

      • Kanjere kampiru komanso zofufumitsa (31-33)

      • Kugwiritsa ntchito mafanizo kunakwaniritsa ulosi (34, 35)

      • Tanthauzo la fanizo la tirigu ndi namsongole (36-43)

      • Chuma chobisika ndi ngale yamtengo wapatali (44-46)

      • Khoka (47-50)

      • Chuma chatsopano ndi chakale (51, 52)

    • Yesu anakanidwa mʼdera lakwawo (53-58)

  • 14

    • Yohane Mʼbatizi anadulidwa mutu (1-12)

    • Yesu anadyetsa anthu 5,000 (13-21)

    • Yesu anayenda pamadzi (22-33)

    • Anachiritsa anthu ku Genesareti (34-36)

  • 15

    • Anadzudzula miyambo ya makolo (1-9)

    • Zodetsa zimachokera mumtima (10-20)

    • Chikhulupiriro cholimba cha mayi wa ku Foinike (21-28)

    • Yesu anachiritsa matenda ambiri (29-31)

    • Yesu anadyetsa anthu 4,000 (32-39)

  • 16

    • Kupempha chizindikiro (1-4)

    • Zofufumitsa za Afarisi ndi Asaduki (5-12)

    • Makiyi a Ufumu (13-20)

      • Mpingo umene udzamangidwe pathanthwe (18)

    • Ananeneratu zokhudza imfa ya Yesu (21-23)

    • Chizindikiro cha ophunzira enieni (24-28)

  • 17

    • Yesu anasintha maonekedwe (1-13)

    • Chikhulupiriro chofanana ndi kanjere ka mpiru (14-21)

    • Yesu ananeneratunso zokhudza imfa yake (22, 23)

    • Anapereka msonkho pogwiritsa ntchito ndalama yamkamwa mwa nsomba (24-27)

  • 18

    • Wamkulu kwambiri mu Ufumu (1-6)

    • Zopunthwitsa (7-11)

    • Fanizo la nkhosa yosochera (12-14)

    • Zimene tingachite kuti tibweze mʼbale wathu (15-20)

    • Fanizo la kapolo wosakhululuka (21-35)

  • 19

    • Ukwati komanso kutha kwa banja (1-9)

    • Mphatso ya kusakwatira (10-12)

    • Yesu anadalitsa ana (13-15)

    • Funso limene wachinyamata wolemera anafunsa (16-24)

    • Zinthu zimene tiyenera kudzimana chifukwa cha Ufumu (25-30)

  • 20

    • Anthu amene ankagwira ntchito mʼmunda wampesa analandira malipiro ofanana (1-16)

    • Yesu ananeneratunso zokhudza imfa yake (17-19)

    • Anapempha kuti adzapatsidwe malo apadera mu Ufumu (20-28)

      • Yesu anapereka dipo kuwombola anthu ambiri (28)

    • Amuna awiri osaona anachiritsidwa (29-34)

  • 21

    • Yesu analowa mumzinda mwaulemerero (1-11)

    • Yesu anayeretsa kachisi (12-17)

    • Anatemberera mtengo wa mkuyu (18-22)

    • Anakayikira ulamuliro wa Yesu (23-27)

    • Fanizo la ana awiri aamuna (28-32)

    • Fanizo la alimi amene anapha anthu (33-46)

      • Mwala wofunika kwambiri wapakona unakanidwa (42)

  • 22

    • Fanizo la phwando laukwati (1-14)

    • Mulungu komanso Kaisara (15-22)

    • Funso lokhudza kuukitsidwa kwa akufa (23-33)

    • Malamulo awiri akuluakulu (34-40)

    • Kodi Khristu ndi mwana wa Davide? (41-46)

  • 23

    • Musamatsanzire alembi ndi Afarisi (1-12)

    • Tsoka kwa alembi ndi Afarisi (13-36)

    • Yesu analirira Yerusalemu (37-39)

  • 24

    • CHIZINDIKIRO CHA KUKHALAPO KWA KHRISTU (1-51)

      • Nkhondo, njala, zivomerezi (7)

      • Uthenga wabwino udzalalikidwa (14)

      • Chisautso chachikulu (21, 22)

      • Chizindikiro cha Mwana wa munthu (30)

      • Mtengo wa mkuyu (32-34)

      • Mofanana ndi masiku a Nowa (37-39)

      • Khalanibe maso (42-44)

      • Kapolo wokhulupirika komanso kapolo woipa (45-51)

  • 25

    • CHIZINDIKIRO CHA KUKHALAPO KWA KHRISTU (1-46)

      • Fanizo la anamwali 10 (1-13)

      • Fanizo la matalente (14-30)

      • Nkhosa komanso mbuzi (31-46)

  • 26

    • Ansembe anakonza chiwembu kuti aphe Yesu (1-5)

    • Yesu anathiridwa mafuta onunkhira (6-13)

    • Pasika womaliza komanso kuperekedwa (14-25)

    • Anayambitsa mwambo wa Chakudya Chamadzulo cha Ambuye (26-30)

    • Ananeneratu kuti Petulo adzamukana (31-35)

    • Yesu anapemphera ku Getsemane (36-46)

    • Yesu anagwidwa (47-56)

    • Anazengedwa mlandu ndi Khoti Lalikulu la Ayuda (57-68)

    • Petulo anakana Yesu (69-75)

  • 27

    • Yesu anaperekedwa kwa Pilato (1, 2)

    • Yudasi anadzimangirira (3-10)

    • Yesu anaonekera kwa Pilato (11-26)

    • Anamuchitira zachipongwe pamaso pa anthu (27-31)

    • Anamukhomerera pamtengo ku Gologota (32-44)

    • Imfa ya Yesu (45-56)

    • Kuikidwa mʼmanda kwa Yesu (57-61)

    • Anakhwimitsa chitetezo pamanda ake (62-66)

  • 28

    • Yesu anaukitsidwa (1-10)

    • Asilikali anapatsidwa ndalama kuti aname (11-15)

    • Analamulidwa kuti azithandiza anthu kuti akhale ophunzira (16-20)