Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

A7-H

Zinthu Zikuluzikulu Zimene Yesu Anachita Ali Padziko Lapansi—Utumiki Womaliza wa Yesu mu Yerusalemu (Gawo 2)

NTHAWI

MALO

ZIMENE ZINACHITIKA

MATEYU

MALIKO

LUKA

YOHANE

Nisani 14

Yerusalemu

Yesu anaulula kuti Yudasi adzamupereka ndipo anamuuza kuti achoke

26:21-25

14:18-21

22:21-23

13:21-30

Anayambitsa mwambo wa Chakudya Chamadzulo (1Akor. 11:23-25)

26:26-29

14:22-25

22:19, 20, 24-30

 

Ananeneratu kuti Petulo adzamukana komanso kuti atumwi adzabalalika

26:31-35

14:27-31

22:31-38

13:31-38

Anati adzatumiza mthandizi; fanizo la mpesa; lamulo loti tizikondana; anapemphera komaliza ndi atumwi ake

     

14:1–17:26

Getsemane

Yesu anavutika maganizo; anaperekedwa ndi kumangidwa

26:30, 36-56

14:26, 32-52

22:39-53

18:1-12

Yerusalemu

Anasi anamufunsa; Kayafa ndi Khoti Lalikulu la Ayuda anamuzenga mlandu; Petulo anamukana

26:57–27:1

14:53–15:1

22:54-71

18:13-27

Yudasi amene anamupereka uja anadzimangirira (Mac. 1:18, 19)

27:3-10

     

Anaonekera kwa Pilato, kenako kwa Herode nʼkubwereranso kwa Pilato

27:2, 11-14

15:1-5

23:1-12

18:28-38

Pilato anayesetsa kuti amumasule koma Ayuda anasankha Baraba; anaweruzidwa kuti aphedwe pomukhomerera pamtengo

27:15-30

15:6-19

23:13-25

18:39–19:16

(c. 3:00 madzulo, Lachisanu)

Gologota

Anafera pamtengo wozunzikirapo

27:31-56

15:20-41

23:26-49

19:16-30

Yerusalemu

Anachotsa mtembo wa Yesu pamtengo nʼkukauika mʼmanda

27:57-61

15:42-47

23:50-56

19:31-42

Nisani 15

Yerusalemu

Ansembe ndi Afarisi anaika alonda pamanda nʼkutsekapo

27:62-66

     

Nisani 16

Yerusalemu ndi madera apafupi; Emau

Yesu anaukitsidwa; anaonekera kwa ophunzira ake ka 5

28:1-15

16:1-8

24:1-49

20:1-25

Pambuyo pa Nisani 16

Yerusalemu; Galileya

Anaonekeranso kwa ophunzira ake kangapo (1Akor. 15:5-7; Mac. 1:3-8); anaphunzitsa; analamula ophunzira ake kuti aphunzitse anthu kukhala ophunzira ake

28:16-20

   

20:26–21:25

Iyari 25

Phiri la Maolivi, pafupi ndi Betaniya

Yesu anakwera kumwamba, tsiku la 40 ataukitsidwa (Mac. 1:9-12)

   

24:50-53