Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

A7-D

Zinthu Zikuluzikulu Zimene Yesu Anachita Ali Padziko Lapansi—Utumiki Waukulu wa Yesu MʼGalileya (Gawo 2)

NTHAWI

MALO

ZIMENE ZINACHITIKA

MATEYU

MALIKO

LUKA

YOHANE

31 kapena 32

Dera la Kaperenao

Yesu anafotokoza mafanizo a Ufumu

13:1-53

4:1-34

8:4-18

 

Nyanja ya Galileya

Analetsa mphepo ali mʼngalawa

8:18, 23-27

4:35-41

8:22-25

 

Dera la Gadara

Anatumiza ziwanda munkhumba

8:28-34

5:1-20

8:26-39

 

Mwina ku Kaperenao

Anachiritsa mayi wamatenda otaya magazi; Anaukitsa mwana wa Yairo

9:18-26

5:21-43

8:40-56

 

Kaperenao (?)

Anachiritsa wosaona ndi wosalankhula

9:27-34

     

Nazareti

Anakanidwanso mumzinda wakwawo

13:54-58

6:1-5

   

Galileya

Ulendo wachitatu wa ku Galileya; anatumiza atumwi kukalalikira

9:35–11:1

6:6-13

9:1-6

 

Tiberiyo

Herode anapha Yohane Mʼbatizi; Anathedwa nzeru atamva za Yesu

14:1-12

6:14-29

9:7-9

 

32, Pasika atayandikira (Yoh. 6:4)

Kaperenao (?); Pafupi ndi Nyanja ya Galileya

Atumwi anabwera kuchokera kolalikira; Yesu anadyetsa amuna 5,000

14:13-21

6:30-44

9:10-17

6:1-13

Pafupi ndi Nyanja ya Galileya; Genesareti

Ankafuna kuveka Yesu ufumu; anayenda panyanja; anachiritsa anthu

14:22-36

6:45-56

 

6:14-21

Kaperenao

Anati iye ndi “chakudya chopatsa moyo”; ambiri anasiya kumutsatira

     

6:22-71

32, Pambuyo pa Pasika

Mwina ku Kaperenao

Anawadzudzula chifukwa cha miyambo

15:1-20

7:1-23

 

7:1

Foinike; Dekapoli

Anachiritsa mwana wa mayi wa ku Foinike; anadyetsa amuna 4,000

15:21-38

7:24–8:9

   

Magadani

Anapereka chizindikiro cha Yona

15:39–16:4

8:10-12