Pitani ku nkhani yake

Baibulo Komanso Sayansi

Kodi Baibulo limagwirizana ndi zimene asayansi amaphunzitsa? Kodi Baibulo limanena zolondola pankhani za sayansi? Werengani zimene asayansi amanena komanso zimene chilengedwe chimasonyeza pankhani imeneyi.

GALAMUKANI!

Kuchuluka kwa Zinthu Zimene DNA Imasunga

Werengani kuti mudziwe mmene DNA ilili chipangizo chapamwamba kwambiri chosungira zinthu.

GALAMUKANI!

Kuchuluka kwa Zinthu Zimene DNA Imasunga

Werengani kuti mudziwe mmene DNA ilili chipangizo chapamwamba kwambiri chosungira zinthu.

Kodi Zinangochitika Zokha?

Laibulale

Kodi Zamoyo Zinachita Kulengedwa?

Zimene mumakhulupirira pa nkhani ya mmene moyo unayambira zimakhudza moyo wanu.

Mmene Moyo Unayambira—Mafunso 5 Ofunika Kwambiri

Onani zimene umboni umanena kenako musankhe nokha kukhulupirira kuti zinthu zinachita kulengedwa kapena zinakhalako zokha.

Zachilengedwe Zimatiphunzitsa za Ulemerero wa Mulungu

Tikamachita chidwi ndi zinthu za m’chilengedwechi, timaphunzira za makhalidwe a Mlengi wathu ndipo zimatithandiza kuti tikhale naye paubwenzi.