Zatsopano pa JW.ORG
KHALANI MASO
N’chifukwa Chiyani Makhalidwe Abwino Alowa Pansi?—Kodi Baibulo Limanena Zotani?
Makhalidwe abwino alowa pansi kwambiri panopa. Baibulo limafotokoza chifukwa chake makhalidwe abwino alowa pansi komanso lili ndi malangizo omwe angathandize anthu kukhala ndi makhalidwe abwino.
ANTHU OKWATIRANA KOMANSO MABANJA
Kodi Tiyambe Kukhala Limodzi Tisanakwatirane?
Anthu ena amaganiza kuti kuyamba kukhala limodzi kaye asanakwatirane kungawathandize kukonzekera banja. Kodi amenewa ndi maganizo abwino kapena pali njira ina yabwino?
ANTHU OKWATIRANA KOMANSO MABANJA
Mungatani Kuti Mupewe Kuthetsa Banja Pambuyo Pokhala Limodzi kwa Zaka Zambiri?
N’chiyani chikuchititsa kuti anthu azithetsa banja pambuyo pokhala limodzi kwa zaka zambiri? Kodi mungatani kuti zimenezi zisakuchitikireni?
NYIMBO ZA BROADCASTING
“M’dziko Labwino”
Kuganizira kwambiri za chiyembekezo chathu kumatithandiza kupirira ngakhale mavuto aakulu.
NSANJA YA OLONDA
Kodi Tingapeze Kuti Malangizo Otithandiza Kusankha Zinthu Mwanzeru?
Phunzirani mmene mungasankhire zinthu mwanzeru zomwe zingadzathandize inuyo ndi banja lanu.
NKHANI ZINA
Kuteteza Akazi—Zimene Baibulo Limanena
Mulungu amaona kuti akazi ayenera kutetezedwa. Onani chifukwa chake amaona choncho komanso zimene adzachite pothetsa nkhanza zonse zimene anthu amachitira akazi.
KHALANI MASO
Kodi Anthu Adzasiya Liti Kumenya Nkhondo?—Zimene Baibulo Limanena
Posachedwapa nkhondo zonse zidzathetsedwa. Baibulo limafotokoza mmene zimenezi zidzachitikire.
NKHANI ZINA
Kodi Choonadi Ndi Chofunikabe Masiku Ano?
Baibulo lingakuthandizeni kudziwa choonadi m’dziko lomwe anthu ambiri akumafalitsa mabodza.