Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

A6-A

Tchati: Aneneri Komanso Mafumu a Yuda ndi Isiraeli (Gawo 1)

Mafumu a mu Ufumu Wakumʼmwera wa Mafuko Awiri a Yuda

997 B.C.E.

Rehobowamu: zaka 17

980

Abiya (Abiyamu): zaka zitatu

978

Asa: zaka 41

937

Yehosafati: zaka 25

913

Yehoramu: zaka 8

c. 906

Ahaziya: chaka chimodzi

c. 905

Mfumukazi Ataliya: zaka 6

898

Yehoasi: zaka 40

858

Amaziya: zaka 29

829

Uziya (Azariya): zaka 52

Mafumu a mu Ufumu Wakumpoto wa Mafuko 10 a Isiraeli

997 B.C.E.

Yerobowamu: zaka 22

c. 976

Nadabu: zaka ziwiri

c. 975

Basa: zaka 24

c. 952

Ela: zaka ziwiri

c. 947

Zimiri: masiku 7 (c. 951)

Omuri ndi Tibini: zaka 4

Omuri (yekha): zaka 8

c. 940

Ahabu: zaka 22

c. 920

Ahaziya: zaka ziwiri

c. 917

Yehoramu: zaka 12

c. 905

Yehu: zaka 28

876

Yehoahazi: zaka 14

c. 862

Yehoahazi ndi Yehoasi: zaka zitatu

c. 859

Yehoasi (yekha): zaka 16

c. 844

Yerobowamu Wachiwiri: zaka 41

  • Mayina a Aneneri

  • Yoweli

  • Eliya

  • Elisa

  • Yona

  • Amosi