Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

Machitidwe a Atumwi

Machaputala

Mitu

  • 1

    • Mawu oyamba opita kwa Teofilo (1-5)

    • Kulalikira mpaka kumalekezero a dziko lapansi (6-8)

    • Yesu anapita kumwamba (9-11)

    • Ophunzira anasonkhana mogwirizana (12-14)

    • Matiya anasankhidwa kuti alowe mʼmalo mwa Yudasi (15-26)

  • 2

    • Anthu analandira mzimu woyera pa Pentekosite (1-13)

    • Nkhani imene Petulo anakamba (14-36)

    • Anthu anatsatira zimene Petulo ananena (37-41)

      • Anthu 3,000 anabatizidwa (41)

    • Akhristu ankachitira zinthu limodzi (42-47)

  • 3

    • Petulo anachiritsa munthu wolumala wopemphapempha (1-10)

    • Nkhani imene Petulo anakamba Pakhonde Lazipilala la Solomo (11-26)

      • “Nthawi yobwezeretsa zinthu zonse” (21)

      • Mneneri ngati Mose (22)

  • 4

    • Petulo ndi Yohane anamangidwa (1-4)

      • Amuna okhulupirira anakwana 5,000 (4)

    • Kuweruzidwa ndi Khoti Lalikulu la Ayuda (5-22)

      • “Ife sitingasiye kulankhula” (20)

    • Anapemphera kuti akhale olimba mtima (23-31)

    • Ophunzira ankagawana zinthu (32-37)

  • 5

    • Hananiya ndi Safira (1-11)

    • Atumwi anachita zizindikiro zambiri (12-16)

    • Anamangidwa nʼkumasulidwa (17-21a)

    • Anapita nawonso ku Khoti Lalikulu la Ayuda (21b-32)

      • ‘Kumvera Mulungu osati anthu’ (29)

    • Malangizo a Gamaliyeli (33-40)

    • Kulalikira kunyumba ndi nyumba (41, 42)

  • 6

    • Amuna 7 anasankhidwa kuti azitumikira (1-7)

    • Sitefano anaimbidwa mlandu wonyoza Mulungu (8-15)

  • 7

    • Zimene Sitefano ananena polankhula ndi Khoti Lalikulu la Ayuda (1-53)

      • Nthawi ya makolo akale (2-16)

      • Mose anali mtsogoleri; Aisiraeli ankalambira mafano (17-43)

      • Mulungu sakhala mu akachisi omangidwa ndi anthu (44-50)

    • Sitefano anaponyedwa miyala (54-60)

  • 8

    • Saulo ankazunza anthu (1-3)

    • Utumiki wa Filipo unkayenda bwino ku Samariya (4-13)

    • Petulo ndi Yohane anatumizidwa ku Samariya (14-17)

    • Simoni ankafuna kugula mzimu woyera (18-25)

    • Nduna ya ku Itiyopiya (26-40)

  • 9

    • Saulo ali pa ulendo wa ku Damasiko (1-9)

    • Hananiya anatumizidwa kuti akathandize Saulo (10-19a)

    • Saulo analalikira za Yesu ku Damasiko (19b-25)

    • Saulo anapita ku Yerusalemu (26-31)

    • Petulo anachiritsa Eneya (32-35)

    • Dolika, yemwe anali wopatsa, anaukitsidwa (36-43)

  • 10

    • Masomphenya a Koneliyo (1-8)

    • Masomphenya a Petulo a nyama zoyeretsedwa (9-16)

    • Petulo anapita kunyumba kwa Koneliyo (17-33)

    • Petulo analalikira uthenga wabwino kwa anthu a mitundu ina (34-43)

      • “Mulungu alibe tsankho” (34, 35)

    • Anthu a mitundu ina analandira mzimu woyera nʼkubatizidwa (44-48)

  • 11

    • Petulo anakapereka lipoti kwa atumwi (1-18)

    • Baranaba ndi Saulo anapita ku Antiokeya wa ku Siriya (19-26)

      • Ophunzira anayamba kutchedwa Akhristu (26)

    • Agabo analosera za njala (27-30)

  • 12

    • Yakobo anaphedwa; Petulo anamangidwa (1-5)

    • Petulo anamasulidwa modabwitsa (6-19)

    • Herode anaphedwa ndi mngelo (20-25)

  • 13

    • Baranaba ndi Saulo anatumizidwa kuti akakhale amishonale (1-3)

    • Utumiki wa ku Kupuro (4-12)

    • Zimene Paulo analankhula ku Antiokeya wa ku Pisidiya (13-41)

    • Ulosi woti ayambe kulalikira kwa anthu a mitundu ina (42-52)

  • 14

    • Okhulupirira anawonjezeka ku Ikoniyo; anayamba kutsutsidwa (1-7)

    • Ankawayesa kuti ndi milungu ku Lusitara (8-18)

    • Paulo anapulumuka atamuponya miyala (19, 20)

    • Analimbikitsa mipingo (21-23)

    • Anabwerera ku Antiokeya wa ku Siriya (24-28)

  • 15

    • Anatsutsana ku Antiokeya pa nkhani ya mdulidwe (1, 2)

    • Nkhaniyi anapita nayo ku Yerusalemu (3-5)

    • Akulu ndi atumwi anakumana kuti akambirane (6-21)

    • Kalata yochokera ku bungwe lolamulira (22-29)

    • Mipingo inalimbikitsidwa ndi kalata (30-35)

    • Paulo ndi Baranaba anasiyana (36-41)

  • 16

    • Paulo anasankha Timoteyo (1-5)

    • Masomphenya a munthu wa ku Makedoniya (6-10)

    • Lidiya anakhala Mkhristu ku Filipi (11-15)

    • Paulo ndi Sila anamangidwa (16-24)

    • Woyangʼanira ndende ndi banja lake anabatizidwa (25-34)

    • Paulo ananena kuti akuluakulu a zamalamulo apepese (35-40)

  • 17

    • Paulo ndi Sila ku Tesalonika (1-9)

    • Paulo ndi Sila ku Bereya (10-15)

    • Paulo ku Atene (16-22a)

    • Zimene Paulo analankhula kubwalo la Areopagi (22b-34)

  • 18

    • Utumiki wa Paulo ku Korinto (1-17)

    • Anabwerera ku Antiokeya wa ku Siriya (18-22)

    • Paulo anachoka ku Galatiya ndi ku Fulugiya (23)

    • Apolo, yemwe ankalankhula mwaluso, anathandizidwa (24-28)

  • 19

    • Paulo ku Efeso; anthu ena anabatizidwanso (1-7)

    • Ntchito yolalikira ya Paulo (8-10)

    • Utumiki unkayenda bwino ngakhale kuti ena ankakhulupirira zamizimu (11-20)

    • Chisokonezo ku Efeso (21-41)

  • 20

    • Paulo ku Makedoniya ndi ku Girisi (1-6)

    • Utiko anaukitsidwa ku Torowa (7-12)

    • Kuchoka ku Torowa kupita ku Mileto (13-16)

    • Paulo anakumana ndi akulu a ku Efeso (17-38)

      • Ankaphunzitsa kunyumba ndi nyumba (20)

      • “Kupatsa kumatichititsa kukhala osangalala kwambiri” (35)

  • 21

    • Ulendo wa ku Yerusalemu (1-14)

    • Anafika ku Yerusalemu (15-19)

    • Paulo anatsatira malangizo a akulu (20-26)

    • Chisokonezo mʼkachisi; Paulo anamangidwa (27-36)

    • Paulo analoledwa kulankhula ndi gulu la anthu (37-40)

  • 22

    • Mawu a Paulo odziteteza pamaso pa gulu la anthu (1-21)

    • Paulo anagwiritsa ntchito mwayi wokhala nzika ya Roma (22-29)

    • Khoti Lalikulu la Ayuda linakumana (30)

  • 23

    • Paulo analankhula pamaso pa Khoti Lalikulu la Ayuda (1-10)

    • Paulo analimbikitsidwa ndi Ambuye (11)

    • Chiwembu chofuna kupha Paulo (12-22)

    • Paulo anapititsidwa ku Kaisareya (23-35)

  • 24

    • Milandu imene Paulo ankaimbidwa (1-9)

    • Paulo anadziteteza pamaso pa Felike (10-21)

    • Mlandu wa Paulo unaimitsidwa kwa zaka ziwiri (22-27)

  • 25

    • Mlandu wa Paulo pamaso pa Fesito (1-12)

      • “Ndikuchita apilo kuti ndikaonekere kwa Kaisara” (11)

    • Fesito anafunsa nzeru kwa Mfumu Agiripa (13-22)

    • Paulo anaonekera kwa Agiripa (23-27)

  • 26

    • Paulo anadziteteza pamaso pa Agiripa (1-11)

    • Paulo anafotokoza mmene anakhalira Mkhristu (12-23)

    • Zimene Fesito ndi Agiripa anachita (24-32)

  • 27

    • Paulo anayenda ulendo wapanyanja wopita ku Roma (1-12)

    • Ngalawa inawonongeka ndi mphepo (13-38)

    • Ngalawa inasweka (39-44)

  • 28

    • Anafika kugombe la ku Melita (1-6)

    • Bambo ake a Papuliyo anachiritsidwa (7-10)

    • Ulendo wa ku Roma (11-16)

    • Paulo analankhula ndi Ayuda ku Roma (17-29)

    • Paulo analalikira molimba mtima kwa zaka ziwiri (30, 31)