Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

Buku la Zefaniya

Machaputala

1 2 3

Mitu

  • 1

    • Tsiku la chiweruzo la Yehova lili pafupi (1-18)

      • Tsiku la Yehova likubwera mofulumira (14)

      • Siliva ndi golide sizingapulumutse munthu (18)

  • 2

    • Funafunani Yehova tsiku la mkwiyo wake lisanafike (1-3)

      • Yesetsani kukhala olungama ndi ofatsa (3)

      • “Mwina mungadzabisike” (3)

    • Kuweruza mitundu yozungulira (4-15)

  • 3

    • Yerusalemu, mzinda wogalukira ndiponso wachinyengo (1-7)

    • Kuweruza ndiponso kubwezeretsa (8-20)

      • Kusintha nʼkuyamba kulankhula chilankhulo choyera (9)

      • Anthu odzichepetsa komanso ooneka onyozeka adzapulumutsidwa (12)

      • Yehova adzakondwera ndi Ziyoni (17)