Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

Buku la Yoweli

Machaputala

1 2 3

Mitu

  • 1

    • Mliri woopsa wa ziwala ndi dzombe (1-14)

    • “Tsiku la Yehova lili pafupi” (15-20)

      • Mneneri anaitana Yehova (19, 20)

  • 2

    • Tsiku la Yehova komanso gulu lalikulu la asilikali ake (1-11)

    • Anawauza kuti abwerere kwa Yehova (12-17)

      • “Ngʼambani mitima yanu” (13)

    • Yehova anayankha anthu ake (18-32)

      • “Ndidzapereka mzimu wanga”  (28)

      • Zodabwitsa kumwamba ndi padziko lapansi (30)

      • Oitana pa dzina la Yehova adzapulumuka (32)

  • 3

    • Yehova adzaweruza mitundu yonse ya anthu (1-17)

      • Chigwa cha Yehosafati (2, 12)

      • Chigwa choweruzira (14)

      • Yehova, malo othawirako a Isiraeli (16)

    • Yehova adzadalitsa anthu ake (18-21)