Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

Buku la Yona

Machaputala

1 2 3 4

Mitu

  • 1

    • Yona ankafuna kuthawa Yehova (1-3)

    • Yehova anayambitsa chimphepo (4-6)

    • Mavuto anayamba chifukwa cha Yona (7-13)

    • Yona anaponyedwa mʼnyanja (14-16)

    • Chinsomba chinameza Yona (17)

  • 2

    • Pemphero la Yona ali mʼmimba mwa chinsomba (1-9)

    • Chinsomba chinalavulira Yona kumtunda (10)

  • 3

    • Yona anamvera Mulungu nʼkupita ku Nineve (1-4)

    • Anthu a ku Nineve analapa atamva uthenga wa Yona (5-9)

    • Mulungu anaganiza zoti asawononge Nineve (10)

  • 4

    • Yona anakwiya ndipo ankafuna kufa (1-3)

    • Yehova anaphunzitsa Yona kukhala wachifundo (4-11)

      • “Kodi pali chifukwa choti ukwiyire choncho?” (4)

      • Anamuphunzitsa pogwiritsa ntchito chomera chamtundu wa mphonda (6-10)