Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

Nyimbo ya Solomo

Machaputala

1 2 3 4 5 6 7 8

Mitu

  • MSULAMI ALI MUMSASA WA MFUMU SOLOMO (1:1–3:5)

    • 1

      • Nyimbo yoposa nyimbo zonse (1)

      • Mtsikana (2-7)

      • Ana aakazi a ku Yerusalemu (8)

      • Mfumu (9-11)

        • “Ife tikupangira zokongoletsa zagolide” (11)

      • Mtsikana (12-14)

        • ‘Wachikondi wanga ali ngati kathumba konunkhira ka mule’ (13)

      • Mʼbusa (15)

        • “Ndiwe wokongola wokondedwa wanga”

      • Mtsikana (16, 17)

        • “Iwenso ndiwe wooneka bwino, wachikondi wanga” (16)

    • 2

      • Mtsikana (1)

        • “Ine ndine duwa chabe”

      • Mʼbusa (2)

        • ‘Wokondedwa wanga ali ngati duwa’

      • Mtsikana (3-14)

        • “Musayese kudzutsa chikondi mwa ine nthawi yake isanakwane” (7)

        • Mawu a mʼbusa (10b-14)

          • “Ndiwe wokongola kwa ine, tiye tizipita” (10b, 13)

      • Azichimwene ake a mtsikana (15)

        • “Tigwirireni nkhandwe”

      • Mtsikana (16, 17)

        • “Wachikondi wanga ndi wanga, ndipo ine ndine wake” (16)

    • 3

      • Mtsikana (1-5)

        • ‘Usiku ndinaganizira za munthu amene ndimamukonda’ (1)

  • MSULAMI ALI KU YERUSALEMU (3:6–8:4)

    • 3

      • Ana aakazi a Ziyoni (6-11)

        • Gulu la anthu limene linkayenda ndi Solomo

    • 4

      • Mʼbusa (1-5)

        • “Ndiwe wokongola wokondedwa wanga” (1)

      • Mtsikana (6)

      • Mʼbusa (7-16a)

        • ‘Watenga mtima wanga, mkwatibwi wanga’ (9)

      • Mtsikana (16b)

    • 5

      • Mʼbusa (1a)

      • Akazi a ku Yerusalemu (1b)

        • ‘Muledzere ndi chikondi!’

      • Mtsikana (2-8)

        • Anafotokoza maloto

      • Ana aakazi a ku Yerusalemu (9)

        • “Kodi wachikondi wakoyo akuposa bwanji achikondi ena onse?”

      • Mtsikana (10-16)

        • “Pa amuna 10,000, iye ndi wooneka bwino kwambiri” (10)

    • 6

      • Ana aakazi a ku Yerusalemu (1)

      • Mtsikana (2, 3)

        • “Wachikondi wanga, ine ndi wake ndipo iye ndi wanga” (3)

      • Mfumu (4-10)

        • “Ndiwe wokongola ngati Tiriza” (4)

        • Mawu a akazi (10)

      • Mtsikana (11, 12)

      • Mfumu (ndi anthu ena) (13a)

      • Mtsikana (13b)

      • Mfumu (ndi anthu ena) (13c)

    • 7

      • Mfumu (1-9a)

        • ‘Mtsikana iwe ndiwe wosangalatsa’ (6)

      • Mtsikana (9b-13)

        • “Wachikondi wangayo, ine ndine wakewake, ndipo iye amalakalaka ineyo” (10)

    • 8

      • Mtsikana (1-4)

        • “Ndikulakalaka ukanakhala mchimwene wanga” (1)

  • MSULAMI WABWERERA KWAWO, WASONYEZA KUTI NDI WOKHULUPIRIKA (8:5-14)

    • 8

      • Azichimwene ake a mtsikana (5a)

        • ‘Kodi ndi ndani amene wakoleka dzanja mʼkhosi mwa wachikondi wake?’

      • Mtsikana (5b-7)

        • “Mofanana ndi Manda, chikondi sichigonja” (6)

      • Azichimwene ake a mtsikana (8, 9)

        • “Akakhala khoma, . . . koma akakhala chitseko, . . .” (9)

      • Mtsikana (10-12)

        • “Ine ndine khoma” (10)

      • Mʼbusa (13)

        • ‘Ndikufuna ndimve mawu akoʼ

      • Mtsikana (14)

        • “Thamanga ngati insa”