SANKHANI Buku la M'Baibulo Genesis Ekisodo Levitiko Numeri Deuteronomo Yoswa Oweruza Rute 1 Samueli 2 Samueli 1 Mafumu 2 Mafumu 1 Mbiri 2 Mbiri Ezara Nehemiya Esitere Yobu Masalimo Miyambo Mlaliki Nyimbo ya Solomo Yesaya Yeremiya Maliro Ezekieli Danieli Hoseya Yoweli Amosi Obadiya Yona Mika Nahumu Habakuku Zefaniya Hagai Zekariya Malaki Mateyu Maliko Luka Yohane Machitidwe Aroma 1 Akorinto 2 Akorinto Agalatiya Aefeso Afilipi Akolose 1 Atesalonika 2 Atesalonika 1 Timoteyo 2 Timoteyo Tito Filimoni Aheberi Yakobo 1 Petulo 2 Petulo 1 Yohane 2 Yohane 3 Yohane Yuda Chivumbulutso Chaputala 1 2 3 4 5 6 7 8 9 10 11 12 13 14 15 16 17 18 19 20 21 22 23 24 25 Buku la 2 Mafumu Machaputala 1 2 3 4 5 6 7 8 9 10 11 12 13 14 15 16 17 18 19 20 21 22 23 24 25 Mitu 1 Eliya analosera za imfa ya Ahaziya (1-18) 2 Eliya anatengedwa ndi mphepo yamkuntho (1-18) Elisa anatenga chovala chauneneri cha Eliya (13, 14) Elisa anachititsa kuti madzi a ku Yeriko akhale abwino (19-22) Zimbalangondo zinapha anyamata a ku Beteli (23-25) 3 Yehoramu, mfumu ya Isiraeli (1-3) Amowabu anagalukira Isiraeli (4-25) Amowabu anagonjetsedwa (26, 27) 4 Elisa anachulukitsa mafuta a mkazi wamasiye (1-7) Mtima wochereza wa mayi wa ku Sunemu (8-16) Mayi anakhala ndi mwana; mwanayo anamwalira (17-31) Elisa anaukitsa mwana (32-37) Elisa anachotsa poizoni mʼchakudya (38-41) Elisa anachulukitsa mikate (42-44) 5 Elisa anachiritsa khate la Namani (1-19) Gehazi wadyera anakhala wakhate (20-27) 6 Elisa anayandamitsa nkhwangwa (1-7) Elisa ndi Asiriya (8-23) Maso a mtumiki wa Elisa anatsegulidwa (16, 17) Asiriya anachititsidwa khungu lamaganizo (18, 19) Mumzinda wa Samariya munali njala chifukwa choti unazunguliridwa (24-33) 7 Elisa analosera za kutha kwa njala (1, 2) Chakudya chinangosiyidwa mumsasa wa Asiriya (3-15) Ulosi wa Elisa unakwaniritsidwa (16-20) 8 Mayi wa ku Sunemu anabwezeredwa malo ake (1-6) Elisa, Beni-hadadi ndi Hazaeli (7-15) Yehoramu, mfumu ya Yuda (16-24) Ahaziya, mfumu ya Yuda (25-29) 9 Yehu anadzozedwa kukhala mfumu ya Isiraeli (1-13) Yehu anapha Yehoramu ndi Ahaziya (14-29) Yezebeli anaphedwa; agalu anadya thupi lake (30-37) 10 Yehu anapha anthu amʼbanja la Ahabu (1-17) Yehonadabu anagwirizana ndi Yehu (15-17) Yehu anapha anthu olambira Baala (18-27) Ulamuliro wa Yehu (28-36) 11 Ataliya analanda ufumu (1-3) Yehoasi anavekedwa ufumu mobisa (4-12) Ataliya anaphedwa (13-16) Yehoyada anasintha zinthu (17-21) 12 Yehoasi mfumu ya Yuda (1-3) Yehoasi anakonza kachisi (4-16) Asiriya anaukira (17, 18) Yehoasi anaphedwa (19-21) 13 Yehoahazi mfumu ya Isiraeli (1-9) Yehoasi mfumu ya Isiraeli (10-13) Elisa anayesa khama la Yehoasi (14-19) Elisa anamwalira; mafupa ake anaukitsa munthu (20, 21) Ulosi womaliza wa Elisa unakwaniritsidwa (22-25) 14 Amaziya, mfumu ya Yuda (1-6) Amaziya anamenyana ndi Aedomu ndi Aisiraeli (7-14) Imfa ya Yehoasi wa ku Isiraeli (15, 16) Imfa ya Amaziya (17-22) Yerobowamu Wachiwiri, mfumu ya Isiraeli (23-29) 15 Azariya, mfumu ya Yuda (1-7) Mafumu omaliza a Yuda: Zekariya (8-12), Salumu (13-16), Menahemu (17-22), Pekahiya (23-26), Peka (27-31) Yotamu, mfumu ya Yuda (32-38) 16 Ahazi, mfumu ya Yuda (1-6) Ahazi anapereka ziphuphu kwa Asuri (7-9) Ahazi anatengera mapulani a guwa la mulungu wonama (10-18) Imfa ya Ahazi (19, 20) 17 Hoshiya, mfumu ya Isiraeli (1-4) Kugonjetsedwa kwa Isiraeli (5, 6) Aisiraeli anapita ku ukapolo chifukwa cha mpatuko (7-23) Anthu a mitundu ina anabweretsedwa mʼmizinda ya ku Samariya (24-26) Ku Samariya kunali zipembedzo zosiyanasiyana (27-41) 18 Hezekiya, mfumu ya Yuda (1-8) Kugonjetsedwa kwa ufumu wa Isiraeli (9-12) Senakeribu anaukira Yuda (13-18) Rabisake ananyoza Yehova (19-37) 19 Hezekiya anapempha thandizo kwa Yehova kudzera mwa Yesaya (1-7) Senakeribu anaopseza Yerusalemu (8-13) Pemphero la Hezekiya (14-19) Yesaya anafotokoza zimene Mulungu anayankha (20-34) Mngelo anapha Asuri 185,000 (35-37) 20 Hezekiya anadwala nʼkuchira (1-11) Anthu anatumidwa kuchokera ku Babulo (12-19) Imfa ya Hezekiya (20, 21) 21 Manase, mfumu ya Yuda; anapha anthu (1-18) Yerusalemu adzawonongedwa (12-15) Amoni, mfumu ya Yuda (19-26) 22 Yosiya, mfumu ya Yuda (1, 2) Malangizo okhudza kukonza kachisi (3-7) Anapeza buku la Chilamulo (8-13) Hulida analosera tsoka (14-20) 23 Yosiya anasintha zinthu (1-20) Anachita chikondwerero cha Pasika (21-23) Zinthu zinanso zimene Yosiya anasintha (24-27) Imfa ya Yosiya (28-30) Yehoahazi, mfumu ya Yuda (31-33) Yehoyakimu, mfumu ya Yuda (34-37) 24 Kugalukira kwa Yehoyakimu komanso imfa yake (1-7) Yehoyakini, mfumu ya Yuda (8, 9) Ayuda oyamba kupita ku Babulo (10-17) Zedekiya, mfumu ya Yuda; anagalukira (18-20) 25 Nebukadinezara anazungulira Yerusalemu (1-7) Yerusalemu ndi kachisi wake anawonongedwa; Ayuda enanso anapita ku Babulo (8-21) Gedaliya anaikidwa kuti azilamulira (22-24) Gedaliya anaphedwa; anthu anathawira ku Iguputo (25, 26) Yehoyakini anamasulidwa ku Babulo (27-30) Yam'mbuyo Yotsatira Sindikizani Patsani ena Patsani ena 2 Mafumu—Zimene Zili Mʼbukuli BAIBULO LA DZIKO LATSOPANO LA MALEMBA OPATULIKA (LOKONZEDWANSO MU 2023) 2 Mafumu—Zimene Zili Mʼbukuli Chichewa 2 Mafumu—Zimene Zili Mʼbukuli https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/1001061100/univ/wpub/1001061100_univ_sqr_xl.jpg nwt 2 Mafumu mas. 640-642