Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

Kalata Yoyamba Yopita kwa Atesalonika

Machaputala

1 2 3 4 5

Mitu

  • 1

    • Moni (1)

    • Kuthokoza chifukwa cha chikhulupiriro cha Atesalonika (2-10)

  • 2

    • Utumiki wa Paulo ku Tesalonika (1-12)

    • Atesalonika analandira mawu a Mulungu (13-16)

    • Paulo ankalakalaka kuona Atesalonika (17-20)

  • 3

    • Paulo anapitiriza kukhala ku Atene podikira lipoti lochokera ku Tesalonika (1-5)

    • Timoteyo anabweretsa lipoti lolimbikitsa (6-10)

    • Anapempherera Atesalonika (11-13)

  • 4

    • Anawachenjeza kuti azipewa chiwerewere (1-8)

    • Muzikondana kwambiri kuposa mmene mukuchitira (9-12)

      • “Musamalowerere nkhani za ena” (11)

    • Amene anafa mwa Khristu adzakhala oyambirira kuuka (13-18)

  • 5

    • Kubwera kwa tsiku la Yehova (1-5)

      • “Bata ndi mtendere!” (3)

    • Khalanibe maso komanso oganiza bwino (6-11)

    • Kuwalimbikitsa (12-24)

    • Moni womaliza (25-28)