Pitani ku nkhani yake

Zochitika pa Moyo wa a Mboni za Yehova

A Mboni za Yehova amayesetsa kulola kuti Baibulo lomwe ndi Mawu a Mulungu lizitsogolera maganizo, zoyankhula ndi zochita zawo. Onani mmene lawathandizira pa moyo wawo komanso pa moyo wa anthu ena.

ZOCHITIKA PA MOYO

Amalimbikitsa Ena Ngakhale Kuti Akudwala

Posafuna kumangokhalira kudzimvera chisoni, Clodean anapemphera kwa Mulungu kuti amupatse mphamvu zoti azitha kulimbikitsa anthu ena.

ZOCHITIKA PA MOYO

Amalimbikitsa Ena Ngakhale Kuti Akudwala

Posafuna kumangokhalira kudzimvera chisoni, Clodean anapemphera kwa Mulungu kuti amupatse mphamvu zoti azitha kulimbikitsa anthu ena.

Baibulo Limasintha Anthu