Pitani ku nkhani yake

Baibulo Komanso Sayansi

Kodi Baibulo limagwirizana ndi zimene asayansi amaphunzitsa? Kodi Baibulo limanena zolondola pankhani za sayansi? Werengani zimene asayansi amanena komanso zimene chilengedwe chimasonyeza pankhani imeneyi.

KUYANKHA MAFUNSO A M’BAIBULO

Kodi Mulungu Anayamba Liti Kulenga Zinthu?

Yankho lake lagona pa mmene mawu akuti “pachiyambi” ndiponso “tsiku” anawagwiritsira ntchito m’buku la Genesis.

KUYANKHA MAFUNSO A M’BAIBULO

Kodi Mulungu Anayamba Liti Kulenga Zinthu?

Yankho lake lagona pa mmene mawu akuti “pachiyambi” ndiponso “tsiku” anawagwiritsira ntchito m’buku la Genesis.

Kodi Zinangochitika Zokha?

Laibulale

Kodi Zamoyo Zinachita Kulengedwa?

Zimene mumakhulupirira pa nkhani ya mmene moyo unayambira zimakhudza moyo wanu.

Mmene Moyo Unayambira—Mafunso 5 Ofunika Kwambiri

Onani zimene umboni umanena kenako musankhe nokha kukhulupirira kuti zinthu zinachita kulengedwa kapena zinakhalako zokha.

Zachilengedwe Zimatiphunzitsa za Ulemerero wa Mulungu

Tikamachita chidwi ndi zinthu za m’chilengedwechi, timaphunzira za makhalidwe a Mlengi wathu ndipo zimatithandiza kuti tikhale naye paubwenzi.