Pitani ku nkhani yake

Kukhulupirira Mulungu

Chikhulupiriro n’champhamvu kwambiri ndipo chimathandiza munthu kukhala ndi mtendere wam’maganizo panopa komanso chiyembekezo chodalirika cham’tsogolo. Ngati simunakhulupirirepo Mulungu, munasiya kumukhulupirira kapenanso mukufuna kulimbitsa chikhulupiriro chanu, Baibulo lingakuthandizeni.

Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo—Amuna ndi Akazi Otchulidwa M’Baibulo