Pitani ku nkhani yake

Kulera Ana

Zimene Mungachite Kuti Mukhale Mayi Kapena Bambo Wabwino

Zimene Mungachite Kuti Mukhale Bambo Wabwino

Zimene mukuchita panopa monga mwamuna zimasonyeza kuti mudzakhala bambo wotani mwana wanu akadzabadwa.

Zimene Makolo Ayenera Kudziwa Zokhudza Kutumiza Mwana Kumalo Osamalira Ana Masana

Dzifunseni mafunso 4 kuti mudziwe ngati kutumiza mwana wanu kumalo osamalira ana kungathandize mwanayo.

Kodi Mungatani Kuti Mukhale Makolo Abwino?

Kodi mungatani kuti ana anu akule bwino?

Kodi Mwana Wanga Akhale ndi Foni?

Dzifunseni mafunso awa kuti mudziwe ngati inuyo ndi mwana wanu muli okonzeka.

Phunzitsani Ana Anu Kugwiritsa Ntchito Foni Mosamala

Ngakhale ana amene amadziwa bwino kugwiritsa ntchito foni amafunika kuphunzitsidwa mmene angaigwiritsire ntchito mosamala.

N’chifukwa Chiyani Kuwerenga ndi Kofunika Kwambiri kwa Ana?​—Mbali Yoyamba: Kodi Zomwe Zingawathandize Ndi Zowerenga Kapena Zoonera?

Ana ambiri amakonda kuonera mavidiyo. Kodi makolo angalimbikitse bwanji ana kuti azikonda kwambiri kuwerenga?

Mmene Mungathandizire Ana Anu kuti Asasokonezeke Ndi Nkhani Zoopsa

Kodi makolo angathandize bwanji ana awo kuti asasokonezeke ndi nkhani zoopsa?

Kuti Banja Liziyenda Bwino​—Kupereka Chitsanzo

Kuti ana anu azitsatira zimene mumawaphunzitsa, zimene mumanena zizigwirizana ndi zimene mumachita.

Zimene Mungachite Ngati Muli ndi Mwana Wolumala

Werengani kuti mumve za mavuto atatu amene mwina mumakumana nawo komanso mmene Baibulo lingakuthandizireni.

Kuphunzitsa

Ubwino wa Masewera Othandiza Kuganiza

N’zothandiza kwambiri poyerekezera ndi masewera a pazipangizo zamakono kapena ochita kukonzedweratu.

Kodi Kuphunzitsa Ana Ntchito Zapakhomo N’kothandiza Bwanji?

Kodi makolo zimakuvutani kuphunzitsa ana anu ntchito zapakhomo? Ngati ndi choncho, werengani nkhaniyi kuti mudziwe mmene kupatsa ana ntchitozi kumawathandizira kudziwa udindo wawo komanso kukhala osangalala.

Ndingatani Ngati Mwana Wanga Akumaboweka?

Ngati mwana wanu ali pakhomo ndipo akusowa zochita, mfundo zotsatirazi zingakuthandizeni kudziwa zoyenera kuchita.

Mmene Mungalerere Ana Anu Kuti Asakhale Odzikonda

Werengani nkhaniyi kuti mudziwe njira zitatu zimene zingathandize kuti ana anu asakhale odzikonda.

Muziphunzitsa Ana Anu Kukhala ndi Mtima Woyamikira

Ngakhale ana aang’ono akhoza kuphunzira kunena kuti zikomo munthu wina akawachitira zabwino.

Muziwaphunzitsa Kufunika Kokhala ndi Makhalidwe Abwino

Ana amene aphunzitsidwa makhalidwe abwino amakhala ndi tsogolo labwino.

Muziwaphunzitsa Kukhala Odalirika

Kodi ndi nthawi iti imene mwana angaphunzire kukhala wodalirika, pamene ali wamng’ono kapena atakula?

Zimene Mungachite Pophunzitsa Mwana Wanu

Muyenera kuthandiza ana kumvetsa malamulo anu komanso zifukwa zimene mumawalangira.

Muziwaphunzitsa Kukhala Opirira

Ana amene amaphunzira kukhala opirira amatha kulimbana ndi mavuto omwe angakumane nawo.

Mmene Mungathandizire Ana Anu Akamalephera Zinazake

Kulakwa si nkhani yachilendo. Muziwathandiza kuti asamabise zomwe zachitikazo komanso kuti asamadzione kuti ndi olephera.

Mungathandize Bwanji Mwana Wanu Kuti Azikhoza Bwino Kusukulu?

Werengani nkhaniyi kuti muone zimene zingakuthandizeni kudziwa vuto lomwe likuchititsa mwana wanu kuti asamakhoze bwino komanso mmene mungamuthandizire.

Kodi Ndingatani Ngati Nditamva Kuti Mwana Wanga Amavutitsidwa ndi Anzake?

Werengani nkhaniyi kuti mupeze mfundo 4 zomwe zingamuthandize kudziwa zoyenera kuchita akamavutitsidwa.

Muziyamikira Ana Anu

Kuyamikira mwana akachita khama n’kothandiza kwambiri.

Zimene Mungachite Mwana Akatsala Pang’ono Kutha Msinkhu

Mfundo 5 za m’Baibulo zomwe zingathandize makolo panthawi imene mwana wawo akukumana ndi mavuto chifukwa cha kusintha kwa thupi lake.

Kodi Mungayankhe Bwanji Mwana Wanu Atakufunsani za Imfa?

Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zinthu 4 zimene mungachite pothandiza mwana wanu kudziwa zokhudza imfa komanso mmene mungamuthandizire kupirira wachibale akamwalira.

Kodi Mungatani Kuti Muziphunzitsa Ana Anu Mogwira Mtima?

Kodi mungatani kuti muziphunzitsa ana anu mogwira mtima mfundo za m’Baibulo?

Mmene Mungauzire Mwana Wanu za Kuipa Kosankhana Mitundu

Mukamaphunzitsa mwana wanu za kuipa kosankhana mitundu mogwirizana ndi msinkhu wake, mudzamuthandiza kuti asatengere maganizo olakwika omwe anthu ambiri ali nawo.

Kodi Makolo Angatani Kuti Aphunzitse Ana Awo Nkhani Zokhudza Kugonana?

M’Baibulo muli mfundo zambiri zimene zingakuthandizeni mukafuna kuphunzitsa ana anu mmene angadzitetezere kwa anthu ogwiririra.

Kuphunzitsa Mwana Wanu Nkhani Zokhudza Kugonana

Masiku ano ana akumaona ndiponso kumva zinthu zokhudza kugonana ali aang’ono kwambiri. Kodi muyenera kudziwa zotani? Kodi mungachite chiyani kuti muziteteza ana anu?

Tetezani Ana Anu

Kalebe ndi sofiya akuphunzira zimene angachite kuti akhale otetezeka.

Mmene Mungathandizire Ana Anu pa Nkhani ya Mowa

Kodi ndi liti pamene makolo angayambe kukambirana ndi ana awo zokhudza mowa ndipo angakambirane nawo bwanji?

Malangizo

Phunzitsani Ana Anu Kuti Akhale Odziletsa

Kupatsa ana anu chilichonse chimene akufuna kungawalepheretse kuphunzira makhalidwe ofunika.

Mungaphunzitse Bwanji Ana Anu Kukhala Odzichepetsa?

Muziphunzitsa mwana kukhala wodzichepetsa popanda kum’pangitsa kudziona ngati wachabechabe.

N’chifukwa Chiyani Ana a Masiku Ano Safuna Kuuzidwa Zochita?

Kodi zomwe akatswiri ankanena zaka za m’ma 1960 zikukhudzabe mmene makolo ambiri amalerera ana awo masiku ano?

Kodi Mungatani Kuti Muzilangiza Bwino Ana Anu?

Baibulo limatchula zinthu zitatu zimene makolo ayenera kuchita polangiza ana.

Mungaphunzitse Bwanji Mwana Wanu Kuti Azikumverani?

Kodi inuyo simugwirizana ndi mwana wanu ndipo nthawi zambiri mumangochita zomwe mwanayo akufuna? M’nkhaniyi muli mfundo 5 zomwe zingathandize makolo kulera bwino ana awo.

Kudziletsa N’kofunika Kwambiri

N’chifukwa chiyani kudziletsa n’kofunika, ndipo tingatani kuti tikhale ndi khalidwe limeneli?

Muziwaphunzitsa Kukhala Odzichepetsa

Kuphunzitsa ana anu kukhala odzichepetsa kungawathandize panopo komanso m’tsogolo akadzakula.

Kodi Mungatani Kuti Musamangopatsa Mwana Wanu Chilichonse Chimene Akufuna?

Mungatani ngati mwakaniza mwana wanu zinazake, iye n’kuyamba kuvuta kapena kuchonderera pofuna kudziwa ngati mwatsimikizadi?

Zimene Mungachite Mwana Akayamba Kuvuta

Kodi mungachite chiyani mwana wanu atayamba kuvuta? Baibulo lili ndi malangizo omwe angakuthandizeni kuthana ndi vuto limeneli.

Zimene Mungachite Ngati Mwana Wanu Amanama

Kodi mungatani ngati mwana wanu wanama? Nkhaniyi ikufotokoza malangizo a m’Baibulo amene angakuthandizeni kuphunzitsa mwana wanu kufunika kunena zoona.