Pitani ku nkhani yake

Kulera Ana Achinyamata

Kulankhulana

Zimene Mungachite Kuti Muzimasukirana ndi Mwana Wanu

Kodi mumakhumudwa kwambiri chifukwa cholephera kulankhulana bwino ndi mwana wanu? Kodi n’chiyani chimene chimachititsa kuti muzivutika kulankhulana naye?

Kodi Mungatani Kuti Musamakangane ndi Mwana Wanu?

Mwana wanu akulimbana ndi kuti apeze mfundo zimene aziyendera pa moyo wake ndipo zimenezi zingatheke ngati inuyo mutamamulola kufotokoza maganizo ake. Kodi mungamuthandize bwanji?

Ngati Mwana Wanu Wamkazi Akuvutika Maganizo

Atsikana ambiri amavutika ndi zimene zimachitika akamakula. Kodi makolo angawathandize bwanji akamavutika maganizo chifukwa cha zimenezi?

Malangizo Komanso Kuphunzitsa

Mwana Wanu Wachinyamata Akachita Zinthu Zokuchititsani Kusiya Kumukhulupirira

Musafulumire kuganiza kuti mwana wanu wachinyamata waganiza zoti asamakumvereni. Mukhoza kumuthandiza kuti ayambirenso kuchita zinthu mokhulupirika.

Mmene Mungalangizire Ana Anu

N’chifukwa chiyani zimakhala zosavuta kuti ana azigwirizana kwambiri ndi anzawo kuposa makolo awo?

Zimene Mungachite Kuti Mwana Wanu Azikumverani

Cholinga cha chilango ndi kuphunzitsa. Mfundo za m’Baibulo zingakuthandizeni kuti muphunzitse mwana wanu kumvera.

Mungathandize Bwanji Mwana Wanu Kuti Azikhoza Bwino Kusukulu?

Werengani nkhaniyi kuti muone zimene zingakuthandizeni kudziwa vuto lomwe likuchititsa mwana wanu kuti asamakhoze bwino komanso mmene mungamuthandizire.

Khazikitsani Malamulo oti Mwana Wanu Azitsatira

Kodi mungatani ngati mwana wanu wachinyamata sasangalala ndi malamulo amene munakhazikitsa?

Phunzitsani Ana Anu Kuti Azigwiritsa Ntchito Intaneti Moyenera

Kodi mungatani kuti musamangoikira mwana wanu malamulo koma muzimuphunzitsa kuti azitha kusankha zinthu mwanzeru?

Kodi Mwana Wanga Azigwiritsa Ntchito Intaneti?

Mafunso 4 omwe angakuthandizeni kusankha zoti muchite.

Mmene Mungathandizire Mwana Wanu Amene Amadzivulaza Mwadala

Achinyamata ena amadzivulaza mwadala. N’chiyani chimawachititsa kuti azichita zimenezi? Kodi mungamuthandize bwanji mwana wanu ngati amadzivulaza mwadala?

Kukambirana ndi Mwana Wanu Nkhani Yotumizirana Zinthu Zolaula Pafoni

Musachite kudikira kuti mpaka mwana wanu akumane ndi vuto linalake chifukwa chakuti sanagwiritse ntchito bwino foni yake. Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zimene mungachite kuti mukambirane ndi mwana wanu kuopsa kotumizirana zinthu zolaula.