Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

“Uthenga Wabwino” (Nyimbo ya Msonkhano wa 2024)

“Uthenga Wabwino” (Nyimbo ya Msonkhano wa 2024)

(Luka 2:10)

Pangani Dawunilodi

  1. 1. Tilemekeze M’lungu.

    Amatikonda.

    Anatumiza Mwana wake

    Kudzatipatsa

    Chiyembekezochi.

    (KOLASI)

    Uthengawu ndi

    Wosangalatsa.

    Ndi wabwinodi.

    Tilalikire

    Za uthengawu.

    Khristu wabadwa,

    Mpulumutsi wathu.

  2. 2. Azidzalamulira

    Mwachilungamo.

    Abweretsa Paradaiso

    Ndipo Ufumu

    Wakewo sudzatha.

    (KOLASI)

    Uthengawu ndi

    Wosangalatsa.

    Ndi wabwinodi.

    Tilalikire

    Za uthengawu.

    Khristu wabadwa,

    Mpulumutsi wathu.

    (KOLASI)

    Uthengawu ndi

    Wosangalatsa.

    Ndi wabwinodi.

    Tilalikire

    Za uthengawu.

    Khristu wabadwa,

    Mpulumutsi wathu.