Zatsopano pa JW.ORG
NDANDANDA YA UTUMIKI KOMANSO MOYO WATHU WACHIKHRISTU
September–October 2024
KHALANI MASO
N’chifukwa Chiyani Makhalidwe Abwino Alowa Pansi?—Kodi Baibulo Limanena Zotani?
Makhalidwe abwino alowa pansi kwambiri panopa. Baibulo limafotokoza chifukwa chake makhalidwe abwino alowa pansi komanso lili ndi malangizo omwe angathandize anthu kukhala ndi makhalidwe abwino.
ANTHU OKWATIRANA KOMANSO MABANJA
Kodi Tiyambe Kukhala Limodzi Tisanakwatirane?
Anthu ena amaganiza kuti kuyamba kukhala limodzi kaye asanakwatirane kungawathandize kukonzekera banja. Kodi amenewa ndi maganizo abwino kapena pali njira ina yabwino?
ANTHU OKWATIRANA KOMANSO MABANJA
Mungatani Kuti Mupewe Kuthetsa Banja Pambuyo Pokhala Limodzi kwa Zaka Zambiri?
N’chiyani chikuchititsa kuti anthu azithetsa banja pambuyo pokhala limodzi kwa zaka zambiri? Kodi mungatani kuti zimenezi zisakuchitikireni?
NYIMBO ZA BROADCASTING
“M’dziko Labwino”
Kuganizira kwambiri za chiyembekezo chathu kumatithandiza kupirira ngakhale mavuto aakulu.