Nyuzi
NKHANI ZATSOPANO
Ciunikilo Na. 3 ca Bungwe Lolamulila mu 2024
Mu ciunikilo cino, tikambilana mfundo za m’Baibo zimene zingatithandize kupanga zisankho pa nkhani ya kavalidwe na kudzikongoletsa.
NKHANI ZATSOPANO
Ciunikilo Na. 3 ca Bungwe Lolamulila mu 2024
Mu ciunikilo cino, tikambilana mfundo za m’Baibo zimene zingatithandize kupanga zisankho pa nkhani ya kavalidwe na kudzikongoletsa.
Ciunikilo Na. 2 ca Bungwe Lolamulila mu 2024
Mu ciunikilo cino, tione mmene Atate wathu Yehova amaonetsela kuti “akufuna kuti anthu onse alape.” (2 Pet. 3:9 Tionenso masinthidwe amene apangidwa pa nkhani ya mavalidwe athu pamene tili ku misonkhano ya mpingo kapena ikulu-ikulu.
Ciunikilo Na. 1 ca Bungwe Lolamulila mu 2024
Onani mmene kukonda anthu kumatithandizila kukhala okangalika mu utumiki.
Ciunikilo Na. 8 ca Bungwe Lolamulila mu 2023
Dziŵani mmene timaonetsela kuti ndife atumiki a Mulungu pa zisankho zathu pa nkhani ya kavalidwe na kudzikongoletsa. Komanso onani zimene mungacite kuti musungitse mtendele mu mpingo.
Ciunikilo Na. 7 ca Bungwe Lolamulila mu 2023
Imvani za buku latsopano lakuti Malemba Othandiza pa Umoyo Wathu wa Cikhristu komanso lemba la caka ca 2024.
Ciunikilo Na. 6 ca Bungwe Lolamulila mu 2023
Mu ciunikilo cino, wa m’Bungwe Lolamulila agaŵana nafe nkhani yolimbikitsa ya Negede Teklemariam.
Ciunikilo Na. 5 ca Bungwe Lolamulila mu 2023
Mu ciunikilo cino, wa m’Bungwe Lolamulila aonetsa vidiyo yolimbikitsa ya Dennis Christensen na mkazi wake Irina.
Ciunikilo Na. 4 ca Bungwe Lolamulila mu 2023
Mu lipoti lino, wa m’Bungwe Lolamulila atithandiza kuyembekezela mwacidwi misonkhano yacigawo ya pamasompamaso komanso afotokoza mmene Yehova amatetezela anthu ake mwauzimu.
Ciunikilo Na. 3 ca Bungwe Lolamulila mu 2023
M’bale wa m’Bungwe lolamulila ationetsa mmene abale na alongo athu akupangila Yehova kukhala pothaŵilapo pawo mosasamala kanthu za mavuto aakulu amene akukumana nawo.
Ciunikilo Na. 2 ca Bungwe Lolamulila mu 2023
Mu lipoti lino, wa m’Bungwe Lolamulila atiunikila mmene zinthu zilili kwa abale athu ku Türkiye komanso muli mbali yolimbikitsa yofunsa mafunso.
Ciunikilo Na. 1 ca Bungwe Lolamulila mu 2023#1
Tikulimbikitsani kuonelela ciunikilo ici kuti mumve zilengezo zosangalatsa zokhudza nchito yomanga ku Ramapo komanso nchito za apainiya athu.
Ciunikilo Na. 8 ca Bungwe Lolamulila mu 2022
Wa m’Bungwe Lolamulila akutilimbikitsa kukhala okonzeka kusintha galeta la Yehova likamayenda.
Ciunikilo Na. 6 ca Bungwe Lolamulila mu 2022
Wa m’Bungwe Lolamulila akupeleka lipoti la zocitika zosangalatsa zaposacedwa komanso kulengeza lemba la caka ca 2023.
Ciunikilo Na. 5 ca Bungwe Lolamulila mu 2022
Wa m’Bungwe Lolamulila akufotokoza zimene zinathandiza abale athu kupilila cizunzo mu ulamulilo wakale wa Soviet Union, ndipo akutitsimikizila kuti Yehova adzatithandiza nthawi zonse.
Ciunikilo Na. 4 ca Bungwe Lolamulila mu 2022
Wa m’Bungwe Lolamulila akutilimbikitsa kupilila mayeso mokhulupilika komanso mwacimwemwe potengela citsanzo ca abale athu a kum’mawa kwa Europe.