Onani zimene zilipo

Nyuzi

 

NKHANI ZATSOPANO

Ciunikilo Na. 3 ca Bungwe Lolamulila mu 2024

Mu ciunikilo cino, tikambilana mfundo za m’Baibo zimene zingatithandize kupanga zisankho pa nkhani ya kavalidwe na kudzikongoletsa.

NKHANI ZATSOPANO

Ciunikilo Na. 3 ca Bungwe Lolamulila mu 2024

Mu ciunikilo cino, tikambilana mfundo za m’Baibo zimene zingatithandize kupanga zisankho pa nkhani ya kavalidwe na kudzikongoletsa.

Ciunikilo Na. 2 ca Bungwe Lolamulila mu 2024

Mu ciunikilo cino, tione mmene Atate wathu Yehova amaonetsela kuti “akufuna kuti anthu onse alape.” (2 Pet. 3:9 Tionenso masinthidwe amene apangidwa pa nkhani ya mavalidwe athu pamene tili ku misonkhano ya mpingo kapena ikulu-ikulu.

Ciunikilo Na. 1 ca Bungwe Lolamulila mu 2024

Onani mmene kukonda anthu kumatithandizila kukhala okangalika mu utumiki.

2023-12-15

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Ciunikilo Na. 8 ca Bungwe Lolamulila mu 2023

Dziŵani mmene timaonetsela kuti ndife atumiki a Mulungu pa zisankho zathu pa nkhani ya kavalidwe na kudzikongoletsa. Komanso onani zimene mungacite kuti musungitse mtendele mu mpingo.

2023-10-20

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Ciunikilo Na. 7 ca Bungwe Lolamulila mu 2023

Imvani za buku latsopano lakuti Malemba Othandiza pa Umoyo Wathu wa Cikhristu komanso lemba la caka ca 2024.

2023-08-25

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Ciunikilo Na. 6 ca Bungwe Lolamulila mu 2023

Mu ciunikilo cino, wa m’Bungwe Lolamulila agaŵana nafe nkhani yolimbikitsa ya Negede Teklemariam.

2023-07-31

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Ciunikilo Na. 5 ca Bungwe Lolamulila mu 2023

Mu ciunikilo cino, wa m’Bungwe Lolamulila aonetsa vidiyo yolimbikitsa ya Dennis Christensen na mkazi wake Irina.

2023-06-01

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Ciunikilo Na. 4 ca Bungwe Lolamulila mu 2023

Mu lipoti lino, wa m’Bungwe Lolamulila atithandiza kuyembekezela mwacidwi misonkhano yacigawo ya pamasompamaso komanso afotokoza mmene Yehova amatetezela anthu ake mwauzimu.

2023-06-01

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Ciunikilo Na. 3 ca Bungwe Lolamulila mu 2023

M’bale wa m’Bungwe lolamulila ationetsa mmene abale na alongo athu akupangila Yehova kukhala pothaŵilapo pawo mosasamala kanthu za mavuto aakulu amene akukumana nawo.

2023-03-14

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Ciunikilo Na. 2 ca Bungwe Lolamulila mu 2023

Mu lipoti lino, wa m’Bungwe Lolamulila atiunikila mmene zinthu zilili kwa abale athu ku Türkiye komanso muli mbali yolimbikitsa yofunsa mafunso.

2023-01-18

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Ciunikilo Na. 1 ca Bungwe Lolamulila mu 2023#1

Tikulimbikitsani kuonelela ciunikilo ici kuti mumve zilengezo zosangalatsa zokhudza nchito yomanga ku Ramapo komanso nchito za apainiya athu.

2022-12-08

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Ciunikilo Na. 8 ca Bungwe Lolamulila mu 2022

Wa m’Bungwe Lolamulila akutilimbikitsa kukhala okonzeka kusintha galeta la Yehova likamayenda.

2022-09-05

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Ciunikilo Na. 6 ca Bungwe Lolamulila mu 2022

Wa m’Bungwe Lolamulila akupeleka lipoti la zocitika zosangalatsa zaposacedwa komanso kulengeza lemba la caka ca 2023.

2022-07-28

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Ciunikilo Na. 5 ca Bungwe Lolamulila mu 2022

Wa m’Bungwe Lolamulila akufotokoza zimene zinathandiza abale athu kupilila cizunzo mu ulamulilo wakale wa Soviet Union, ndipo akutitsimikizila kuti Yehova adzatithandiza nthawi zonse.

2022-06-08

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Ciunikilo Na. 4 ca Bungwe Lolamulila mu 2022

Wa m’Bungwe Lolamulila akutilimbikitsa kupilila mayeso mokhulupilika komanso mwacimwemwe potengela citsanzo ca abale athu a kum’mawa kwa Europe.