Nkhani Zaposacedwa Zimene Zinaonekela pa Tsamba Loyamba
Kufuna-funa Coonadi
Baibo imapeleka mayankho a zoona pa mafunso ena ofunika kwambili pa umoyo.
Kodi Nkhondo Zidzatha Liti?—Kodi Baibo Ikutipo Ciyani?
Posacedwa, nkhondo zonse zidzatha. Baibo imafotokoza mmene nkhondo zidzathela.
Mafunso 5 Pankhani ya Mavuto Ayankhidwa.
Kuphunzila Baibo kungakuthandizeni kupeza citonthozo tsoka likagwa.
Pezani Thandizo pa Nkhawa Zanu
Anthu ambili amavutika na nkhawa. Komabe, pali zambili zimene mungacite kuti mupeze thandizo lofunikila.
Kodi Mulungu Wasankha Ndani Kukhala Wolamulila?
M’mbili yonse ya anthu, munthu mmodzi cabe ndiye wakwanilitsa ziyenelezo zokhala wolamulila wa boma la Ufumu wa Mulungu.
Kodi Kuli Mankhwala Othetsela Tsankho?
Kuthetsa tsankho kufunika kuyambila mu mtima na m’maganizo mwathu. Onani mfundo zisanu zimene zingakuthandizeni kuthetsa tsankho.