Onani zimene zilipo

Nkhani Zaposacedwa Zimene Zinaonekela pa Tsamba Loyamba

 

Kufuna-funa Coonadi

Baibo imapeleka mayankho a zoona pa mafunso ena ofunika kwambili pa umoyo.

Kodi Nkhondo Zidzatha Liti?—Kodi Baibo Ikutipo Ciyani?

Posacedwa, nkhondo zonse zidzatha. Baibo imafotokoza mmene nkhondo zidzathela.

Kodi Aramagedo Idzayambila ku Israel?

Kodi Baibo Ikutipo Ciyani?

 

Pindulani na Nsembe ya Yesu

Ganizilani zinthu ziŵili zofunika izi zimene muyenela kucita.

 

Mafunso 5 Pankhani ya Mavuto Ayankhidwa.

Kuphunzila Baibo kungakuthandizeni kupeza citonthozo tsoka likagwa.

Pezani Thandizo pa Nkhawa Zanu

Anthu ambili amavutika na nkhawa. Komabe, pali zambili zimene mungacite kuti mupeze thandizo lofunikila.

Kodi Mulungu Wasankha Ndani Kukhala Wolamulila?

M’mbili yonse ya anthu, munthu mmodzi cabe ndiye wakwanilitsa ziyenelezo zokhala wolamulila wa boma la Ufumu wa Mulungu.

 

Kodi Kuli Mankhwala Othetsela Tsankho?

Kuthetsa tsankho kufunika kuyambila mu mtima na m’maganizo mwathu. Onani mfundo zisanu zimene zingakuthandizeni kuthetsa tsankho.