Pitani ku nkhani yake

Zoti Muchite Pophunzira Baibulo

Zimene Mungachite Kuti Mupeze Anzanu Odalirika

Mungaphunzire zambiri pa nkhani ya Yonatani ndi Davide. Koperani nkhani ya m’Baibuloyi, iwerengeni, ndipo muiganizire mozama n’kuona mmene ingakuthandizireni.