Pitani ku nkhani yake

ZOTI MUCHITE POPHUNZIRA BAIBULO

Muzilandira Uphungu Modzichepetsa

Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zimene Davide anachita polapa tchimo limene anachita ndi Bati-seba, komanso chifukwa chake Yehova anamukhululukira. Koperani nkhani ya m’Baibuloyi, iwerengeni, ndipo muiganizire mozama n’kuona mmene ingakuthandizireni.