Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

Mmene Mungaigwiritsire Ntchito pa Windows 8 Kapena pa Windows Phone 8

Mmene Mungaigwiritsire Ntchito pa Windows 8 Kapena pa Windows Phone 8

JW Library ndi pulogalamu yovomerezeka imene inapangidwa ndi a Mboni za Yehova. Pulogalamuyi ili ndi Mabaibulo osiyanasiyana komanso mabuku ndi timabuku tothandiza pophunzira Baibulo.

 

 

M'CHIGAWO ICHI

Mmene Mungaikire JW Library M’chipangizo Chanu Ngati Simukuipeza ku App Store​​—Windows

Ngati simungathe kuika JW Library m’chipangizo chanu chokhala ndi pulogalamu ya Windows pa app store yovomerezeka, mukhoza kuika nokha pogwiritsa ntchito mafailo a Windows oikira JW Library.