Pitani ku nkhani yake

Phunzitsani Ana Anu

Nkhani za m’Baibulo zino zalembedwa m’mawu osavuta kumva n’cholinga chothandiza makolo kuphunzitsa ana awo mfundo za m’Baibulo zomwe n’zothandiza. Nkhanizi zalembedwa m’njira yakuti makolo aziwerenga pamodzi ndi ana awo.