Pitani ku nkhani yake

Mawu a Mulungu Ayamba Kuwafika Pamtima

Mawu a Mulungu Ayamba Kuwafika Pamtima

Buku la Mateyu linatulutsidwa m’Chinenero Chamanja cha ku Japan. Onani mmene kukhala ndi Baibulo m’chinenero chimene munthu amamva bwino kulili kwa mtengo wapatali.