Mboni za Yehova Padziko Lonse

Sierra Leone

  • M’mphepete mwa Nyanja, mumzinda wa Freetown ku Sierra Leone​—Akuitanira munthu wa m’dera lawo ku Nyumba ya Ufumu kuti akasonkhane nawo

Mfundo Zachidule—Sierra Leone

  • 8,472,000—Chiwerengero cha anthu
  • 2,564—Chiwerengero cha Mboni za Yehova
  • 42—Mipingo
  • Pa anthu 3,621 alionse pali wa Mboni za Yehova m’modzi

NSANJA YA OLONDA (YOPHUNZIRA)

Zinthu Zinkayenda Bwino Chifukwa cha Chikondi

Ngati munayamba posachedwa kufika pa misonkhano ya Mboni za Yehova, mwina mungadabwe kudziwa zimene tinkachita kale.

BUKU LAPACHAKA LA MBONI ZA YEHOVA LA 2014

Sierra Leone ndi Guinea

Nkhaniyi ikusonyeza kuti Mboni za Yehova zakhala zikulalikira uthenga wabwino m’mayiko awiriwa mokhulupirika komanso modzipereka kwambiri.