Mboni za Yehova Padziko Lonse

New Zealand

  • Padoko la Waitemata mumzinda wa Auckland, New Zealand—Akulalikira uthenga wa m’Baibulo kwa msodzi

Mfundo Zachidule—New Zealand

  • 5,199,000—Chiwerengero cha anthu
  • 14,607—Chiwerengero cha Mboni za Yehova
  • 170—Mipingo
  • Pa anthu 360 alionse pali wa Mboni za Yehova m’modzi

GALAMUKANI!

Dziko la New Zealand

Ngakhale kuti dziko New Zealand lili kutali kwambiri, alendo pafupifupi 3 miliyoni amalowa m’dzikoli. Kodi n’chiyani chimawachititsa chidwi alendowa?