Mboni za Yehova Padziko Lonse

Nicaragua

  • Las Pilas, Nicaragua​—Akuphunzitsa pogwiritsa ntchito Baibulo

Mfundo Zachidule—Nicaragua

  • 6,855,000—Chiwerengero cha anthu
  • 28,843—Chiwerengero cha Mboni za Yehova
  • 466—Mipingo
  • Pa anthu 240 alionse pali wa Mboni za Yehova m’modzi

ZOCHITIKA PA MOYO

Madzi Osefukira Anabweretsa Uthenga Wabwino

Kutagwa mvula yamphamvu, anthu a ku Nicaragua anathandizidwa ndi anthu amene sankawayembekezera.

GALAMUKANI!

Dziko la Nicaragua

nyanja yopanda mchere momwe mumapezeka nsomba za m’nyanja zikuluzikulu monga shaki.