Mfundo Zachidule—Sri Lanka
- 22,181,000—Chiwerengero cha anthu
- 7,003—Chiwerengero cha Mboni za Yehova
- 98—Mipingo
- Pa anthu 3,195 alionse pali wa Mboni za Yehova m’modzi
KODI ZOPEREKA ZANU ZIMAGWIRITSIDWA NTCHITO BWANJI?
Zimene Ena Ali Nazo Zimathandizira pa Zimene Ena Akusowa
Kodi mayiko amene amapeza ndalama zochepa amathandizidwa bwanji kuti ntchito yathu iziyenda bwino?
NKHANI
Msonkhano Wapadera Woyamba Kuchitikira ku Sri Lanka
A Mboni za Yehova masauzande ambiri ochokera m’mayiko 7 anakumana ndi abale ndi alongo awo auzimu ku Colombo pamsonkhano wapadera, ndipo umenewu unali woyamba kuchitikira ku Sri Lanka.
Buku Lapachaka la Mboni za Yehova la 2015
Mwambo Wotsegulira Ofesi ya Nthambi ku Sri Lanka
Anthu m’madera osiyanasiyana anatha kuonera pulogalamuyi m’masikirini.