Mfundo Zachidule—Kazakhstan
- 19,899,000—Chiwerengero cha anthu
- 17,287—Chiwerengero cha Mboni za Yehova
- 229—Mipingo
- Pa anthu 1,164 alionse pali wa Mboni za Yehova m’modzi
GALAMUKANI!
Dziko la Kazakhstan
Kale, anthu a ku Kazakhstan ankakonda kusamukasamuka komanso kukhala m’nyumba zotha kuyenda nazo. Kodi zimene anthuwa amachita masiku ano zikusonyeza bwanji kuti amakondabe chikhalidwe cha makolo awo?