Mboni za Yehova Padziko Lonse

Argentina

  • Catamarca, Argentina​—Kukambirana mfundo ya m’Baibulo ndi m’busa woweta nkhosa pafupi ndi mudzi wotchedwa Alumbrera

Mfundo Zachidule—Argentina

  • 46,045,000—Chiwerengero cha anthu
  • 153,751—Chiwerengero cha Mboni za Yehova
  • 1,938—Mipingo
  • Pa anthu 301 alionse pali wa Mboni za Yehova m’modzi

NKHANI

Malo Atsopano Osungirako Zinthu Zakale Atsegulidwa Ku Ofesi ya Nthambi ya Argentina

Malowa ali ndi mbali ziwiri zokhala ndi mitu yakuti, “Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo” komanso “Mawu Anu Adzakhalapo Mpaka Kalekale.”

NKHANI

Ntchito Yayikulu Yolalikira Inachitika pa Nthawi ya Mpikisano wa Olympic wa Masewera a Achinyamata ku Argentina

Abale athu ankagawira mabuku pafupifupi 800 pa tsiku pa nthawi yomwe ankalalikira kwa achinyamata omwe ankachita masewera komanso kwa alendo.