Zimene Baibo Imaphunzitsa
Baibo imapeleka mayankho pa mafunso ofunika kwambili mu umoyo. Malangizo ake akhala odalilika kwa zaka mahandiledi. M’cigawo cino, mudzapeza cifukwa cake mungaidalile Baibo, mmene mungapindulile mukamaiŵelenga, komanso mudzaona mmene malangizo ake alili othandiza.—2 Timoteyo 3:16, 17.
Zimene Zilipo
Phunzilani Baibo
Pemphani kuti wa Mboni adzakucezeleni
Kambilanani nkhani ya m’Baibo na Mboni za Yehova, kapena laŵani maphunzilo a Baibo amene timapeleka.
Kodi Baibo Ingakuthandizeni Bwanji?
Zocita za Ana
Seŵenzetsani zocita zosangalatsazi, zozikika pa Baibo, pophunzitsa ana makhalidwe auzimu.
Kodi Baibo Imati Ciani?
Kuyankha Mafunso a m’Baibo
Pezani mayankho ocokela m’Baibo okhudza Mulungu, Yesu, banja, mavuto komanso ena ambili.