Zimene a Mboni za Yehova Amachita

Ntchito Yathu Yofalitsa Mabuku ndi Zinthu Zina

Tapatsidwa Ntchito Yomasulira “Mawu Opatulika a Mulungu”​—Aroma 3:2

Kwa zaka zambiri, a Mboni za Yehova akhala akugwiritsira ntchito Mabaibulo osiyanasiyana. Koma n’chifukwa chiyani anaganiza zomasulira Baibulo m’Chingelezi chimene anthu amalankhula masiku ano?

Tapatsidwa Ntchito Yomasulira “Mawu Opatulika a Mulungu”​—Aroma 3:2

Kwa zaka zambiri, a Mboni za Yehova akhala akugwiritsira ntchito Mabaibulo osiyanasiyana. Koma n’chifukwa chiyani anaganiza zomasulira Baibulo m’Chingelezi chimene anthu amalankhula masiku ano?