Zimene a Mboni za Yehova Amachita
Ntchito Yathu Yofalitsa Mabuku ndi Zinthu Zina
Tapatsidwa Ntchito Yomasulira “Mawu Opatulika a Mulungu”—Aroma 3:2
Kwa zaka zambiri, a Mboni za Yehova akhala akugwiritsira ntchito Mabaibulo osiyanasiyana. Koma n’chifukwa chiyani anaganiza zomasulira Baibulo m’Chingelezi chimene anthu amalankhula masiku ano?
Tapatsidwa Ntchito Yomasulira “Mawu Opatulika a Mulungu”—Aroma 3:2
Kwa zaka zambiri, a Mboni za Yehova akhala akugwiritsira ntchito Mabaibulo osiyanasiyana. Koma n’chifukwa chiyani anaganiza zomasulira Baibulo m’Chingelezi chimene anthu amalankhula masiku ano?