Mafunso Ofunsidwa Kawirikawiri

N’chifukwa Chiyani a Mboni za Yehova Mumachita Mwambo wa Mgonero wa Ambuye Mosiyana ndi Zipembedzo Zina?

A Mboni za Yehova amaona kuti Mgonero wa Ambuye kapena kuti Chikumbutso cha Imfa ya Khristu ndi mwambo wopatulika kwambiri. Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zimene Baibulo limanena zokhudza mwambowu.

N’chifukwa Chiyani a Mboni za Yehova Mumachita Mwambo wa Mgonero wa Ambuye Mosiyana ndi Zipembedzo Zina?

A Mboni za Yehova amaona kuti Mgonero wa Ambuye kapena kuti Chikumbutso cha Imfa ya Khristu ndi mwambo wopatulika kwambiri. Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zimene Baibulo limanena zokhudza mwambowu.

Kavidiyo: Mboni za Yehova Zikugwira Ntchito Yolalikira Padziko Lonse

Onerani vidiyoyi kuti mudziwe chifukwa chake Mboni za Yehova zikugwira ntchitoyi kwa maola mabiliyoni ambiri komanso m’zinenero zambirimbiri.

N’chifukwa Chiyani Simugwiritsa Ntchito Mtanda Polambira?

Ngakhale kuti ndife Akhristu, sitigwiritsa ntchito mtanda polambira. N’chifukwa chiyani zili choncho?

N’chifukwa Chiyani Simugwiritsa Ntchito Mtanda Polambira?

Ngakhale kuti ndife Akhristu, sitigwiritsa ntchito mtanda polambira. N’chifukwa chiyani zili choncho?

Kodi Ndani Anayambitsa Chipembedzo cha Mboni za Yehova?

Werengani nkhaniyi kuti mudziwe chifukwa chake tikunena kuti Charles Taze Russell si amene anayambitsa chipembedzo cha Mboni za Yehova.

N’chifukwa Chiyani a Mboni za Yehova Amalalikira Anthu Amene Ali Kale ndi Chipembedzo Chawo?

N’chiyani chimatichititsa kulalikira anthu amene ali kale ndi chipembedzo chawo?

Kodi a Mboni za Yehova Amakakamiza Anthu Kuti Asinthe Zipembedzo Zawo?

Kodi a Mboni za Yehova amalalikira n’cholinga chokopa anthu? Kodi iwo amakakamiza anthu kuti alowe chipembedzo chawo?

N’chifukwa Chiyani Simugwiritsa Ntchito Mtanda Polambira?

Ngakhale kuti ndife Akhristu, sitigwiritsa ntchito mtanda polambira. N’chifukwa chiyani zili choncho?

N’chifukwa Chiyani a Mboni za Yehova Mumachita Mwambo wa Mgonero wa Ambuye Mosiyana ndi Zipembedzo Zina?

A Mboni za Yehova amaona kuti Mgonero wa Ambuye kapena kuti Chikumbutso cha Imfa ya Khristu ndi mwambo wopatulika kwambiri. Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zimene Baibulo limanena zokhudza mwambowu.

Kodi a Mboni za Yehova Amapangitsa Kuti Mabanja a Anthu Athe Kapena Alimbe?

Nthawi zina a Mboni za Yehova amanenedwa kuti amapangitsa kuti mabanja a anthu athe. Koma kodi zimenezi n’zoona?

N’chifukwa Chiyani a Mboni za Yehova Mumachita Mwambo wa Mgonero wa Ambuye Mosiyana ndi Zipembedzo Zina?

A Mboni za Yehova amaona kuti Mgonero wa Ambuye kapena kuti Chikumbutso cha Imfa ya Khristu ndi mwambo wopatulika kwambiri. Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zimene Baibulo limanena zokhudza mwambowu.

Kodi a Mboni za Yehova Amapewa Anthu Amene Kale Anali M’chipembedzo Chawo?

Nthawi zina zimakhala zoyenerera kuti munthu achotsedwe mumpingo ndipo zimenezi zimathandiza kuti munthuyo asinthe n’kubwereranso mumpingo.