Achinyamata
ZIMENE ACHINYAMATA AMAFUNSA
N’chifukwa Chiyani Ndiyenera Kupezeka Pamisonkhano ya pa Nyumba ya Ufumu?
Mlungu uliwonse a Mboni za Yehova amakumana kawiri pa nyumba yomwe amalambirira yotchedwa Nyumba ya Ufumu. Kodi kumeneko kumachitika zotani, nanga mungapindule bwanji ngati mutapezeka pamisonkhano yawo?
ZIMENE ACHINYAMATA AMAFUNSA
N’chifukwa Chiyani Ndiyenera Kupezeka Pamisonkhano ya pa Nyumba ya Ufumu?
Mlungu uliwonse a Mboni za Yehova amakumana kawiri pa nyumba yomwe amalambirira yotchedwa Nyumba ya Ufumu. Kodi kumeneko kumachitika zotani, nanga mungapindule bwanji ngati mutapezeka pamisonkhano yawo?
Zimene Achinyamata Amafunsa
Mafunso amene achinyamata amafunsa pa nkhani zokhudza kugonana, anthu ocheza nawo, makolo, sukulu ndi zina zambiri.
Zimene Achinyamata Anzanu Amanena
Mwina mukukumana ndi mavuto omwe simunakumanepo nawo chiyambire. Onani zimene anzanu amachita pothana ndi mavutowo.
Mavidiyo Amakatuni
Kodi munakumanapo ndi vuto linalake limene munaona kuti ndi losatheka kuthana nalo? Mavidiyo amenewa angakuthandizeni kuthana ndi mavuto ambiri omwe achinyamata ambiri amakumana nawo.
Zoti Achinyamata Achite
Mapepalawa angakuthandizeni kuti mukonzekere ndi kulemba zimene mungachite ngati mutakumana ndi vuto limene latchulidwa papepalalo.
Kodi Mukuphunzira Chiyani pa Nkhani ya M’Baibulo Iyi
Nkhani za m’Baibulozi, zomwe mungathe kuzisindikiza zingakuthandizeni ngati mutaziphunzira mozama.
Zokuthandizani Pophunzira
Gwiritsani ntchito zokuthandizani pophunzira kuti musamakaikire zimene mumakhulupirira komanso kuti mudziwe mmene mungazifotokozere kwa ena.